Pitani ku nkhani yake

Kupeza Komanso Kukhala pa Chibwenzi

Kodi Ndine Wokonzeka Kukhala Pachibwenzi?

Mfundo 5 zimene zingakuthandizeni kudziwa ngati muli wokonzeka kukhala pachibwenzi komanso kulowa m’banja

Kodi Kukopana Kuli Ndi Vuto?

Kodi kukopana n’kutani? N’chifukwa chiyani anthu ena amakopana? Kodi kukopana kuli ndi vuto?

Kodi Ndi Mnzanga Chabe Kapena Amandifuna?​—Gawo 1: Kodi Ndikuona Zizindikiro Zotani?

Nkhaniyi ingakuthandizeni kuti mudziwe ngati munthu amakukondani kapena akungofuna kukhala mnzanu chabe.

Kodi Ndi Mnzanga Chabe Kapena Amandifuna?—Gawo 2: Kodi Ndikumukopa?

Kodi mnzanuyu angaganize kuti mukumufuna chibwenzi? Zimene zingakuthandizeni.

Kodi Ndi Chikondi Chenicheni Kapena Kungotengeka Maganizo?

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe tanthauzo la kutengeka maganizo ndiponso chikondi chenicheni.

Kodi Baibulo Limavomereza Kuti Mwamuna ndi Mkazi Azikhalira Limodzi Asanakwatirane?

Malangizo ochokera kwa Mulungu amatithandiza kudziwa zimene tingachite kuti tikhale ndi banja logwirizana ndipo anthu amene amatsatira mfundo zake zinthu zimawayendera bwino nthawi zonse.

Kodi a Mboni za Yehova Amatsatira Mfundo Ziti Zokhudza Kukhala pa Chibwenzi?

Kodi ndi bwino kukhala pa chibwenzi pongofuna kusangalala?

Chikondi Chenicheni

Mfundo za m’Baibulo zingathandize Akhristu posankha munthu woyenera kumanga naye banja, ndiponso zingawathandize kusonyezana chikondi chenicheni akakwatirana.

Kodi Mungatani Ngati Chibwenzi Chatha?

N’chiyani chingakuthandizeni ngati chibwenzi chanu chatha?

Kodi Ndingatani Ngati Chibwenzi Chatha?

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene mungachite ngati mwakhumudwa chifukwa chakuti chibwenzi chatha.