Pitani ku nkhani yake

Malo a Nkhani

 

NKHANI

Vidiyo ya Mboni Yathandiza Makolo Kudziwa Zimene Angachite Kuti Athandize Ana Amene Amavutitsidwa ndi Anzawo

Vidiyo yaifupi yamakatuni yakuti Kodi Mungatani Kuti Anzanu Asiye Kukuvutitsani? Inapangidwa ndi a Mboni za Yehova, ndipo ili ndi malangizo othandiza achinyamata amene amavutitsidwa.

NKHANI

Vidiyo ya Mboni Yathandiza Makolo Kudziwa Zimene Angachite Kuti Athandize Ana Amene Amavutitsidwa ndi Anzawo

Vidiyo yaifupi yamakatuni yakuti Kodi Mungatani Kuti Anzanu Asiye Kukuvutitsani? Inapangidwa ndi a Mboni za Yehova, ndipo ili ndi malangizo othandiza achinyamata amene amavutitsidwa.

2017-07-21

RUSSIA

Akuluakulu a Boma ku Russia Anathokoza Mwapadera a Mboni za Yehova Kuphatikizapo Nzika ya ku Denmark Yomwe ili M’ndende

Akuluakulu mumzinda wa Oryol anathokoza a Mboni za Yehova kuphatikizapo nzika ina ya ku Denmark yomwe ili m’ndende. Iwo anathokoza Amboniwo chifukwa chogwira nawo ntchito yoyeretsa mumzindawo yomwe imachitika chaka chilichonse.

2017-12-28

PHILIPPINES

A Mboni za Yehova Akugwira Ntchito Yokonza Zinthu Zomwe Zinaonongeka ndi Mvula Yamkuntho Yotchedwa Nock-Ten

A Mboni za Yehova akugwira nawo ntchito yokonzanso ndi kumanga nyumba zambirimbiri zomwe zinaonongedwa kapena kugwa ndi mvula yamkuntho ku Philippines chakumapeto kwa 2016.

2017-07-31

UKRAINE

Akuluakulu a Boma ku Ukraine Anakaona Malo ku Ofesi ya Mboni za Yehova Patsiku Lapadera

Kwa nthawi yoyamba kuchokera mu 2001, ofesi ya mboni za Yehova ku Ukraine inakonza tsiku lapadera kuti anthu adzaone ntchito zimene zimachitika paofesiyo ndipo zimene zinachitika pa 2 May, 2017.

2017-07-31

DEMOCRATIC REPUBLIC OF THE CONGO

A Mboni za Yehova Anapereka Chithandizo kwa Anthu Othawa Nkhondo ku Congo

A Mboni za Yehova akupereka chithandizo kwa Akhristu anzawo komanso anthu ena omwe anathawa nkhondo m’chigawo cha Kasai ku Democratic Republic of the Congo.

Mayiko Amene a Mboni za Yehova Akumangidwa Chifukwa Chotsatira Zimene Amakhulupirira

Mayiko amene a Mboni za Yehova akuikidwa m’ndende, mmene nthawi zina amakumana ndi mavuto aakulu, chifukwa chotsatira zimene amakhulupirira komanso ufulu wawo wachibadwidwe.