Pitani ku nkhani yake

Kulankhulana

Kodi Mungatani Kuti Zipangizo Zamakono Zisamakusokonezeni?

Zipangizo zamakono zikhoza kulimbitsa kapena kusokoneza banja lanu. Kodi zimenezi zingachitike bwanji?

Mungatani Kuti Musamakangane Pokambirana Mavuto Anu?

Amuna ndi akazi amafotokoza maganizo awo mosiyana. Kudziwa mfundoyi kungakuthandizeni kuti musamakangane.

Kodi Mungatani Kuti Muzimvetsera Mwamuna Kapena Mkazi Wanu Akamalankhula?

Kumvetsera mwatcheru si luso chabe koma ndi njiranso yosonyezera kuti mnzanuyo mumamukonda. Werengani nkhaniyi kuti mudziwe zimene mungachite kuti muzimvetsera mwamuna kapena mkazi wanu akamalankhula.

Kodi Mungatani Kuti Muzilolerana M’banja?

Mfundo 4 zomwe zingakuthandizeni kuti musamangokangana koma muzipeza njira zothetsera mavuto.

Kodi Mungatani Kuti Muzigwirizana Ndi Anthu a M’banja Lanu?

Kodi mukuganiza kuti Baibulo lingakuthandizeni kuti muzikhala mosangalala m’banja? Werengani nkhaniyi kuti muone malangizo othandiza a m’Baibulo.

Zimene Mwamuna ndi Mkazi Angachite Kuti Asamasiye Kulankhulana Akasemphana Maganizo

Kodi chimachititsa n’chiyani kuti mwamuna ndi mkazi wake asiye kulankhulana, nanga n’chiyani chingathandize kuti athetse kusamvana?

Mungatani Kuti Musamakwiye Mopitirira Malire?

Mukamangokhalira kukwiya kapena kubisa mmene mukumvera, mukhoza kuika moyo wanu pangozi. Kodi mungachite zotani ngati mwamuna kapena mkazi wanu wakukhumudwitsani?

Zimene Mungachite Kuti Musamakangane

Kodi simuchedwa kukangana ndi mwamuna kapena mkazi wanu? Werengani nkhaniyi kuti mudziwe mfundo zimene zingathandize banja lanu.

Kodi Mungapewe Bwanji Kulankhula Mawu Achipongwe?

Kodi mungatani ngati banja lanu lasokonekera chifukwa choti inuyo ndi mkazi kapena mwamuna wanu mumakonda kulankhulana mawu achipongwe?

Kodi Mungatani Ngati Zimakuvutani Kupepesa?

Kodi ndiyenera kupepesabe ngakhale kuti wolakwa si ine?

Kodi Mungatani Kuti Muzikhululukirana?

N’chifukwa chiyani kukhululukirana sikophweka? Werengani nkhani kuti muone mmene Baibulo lingakuthandizireni.

Zimene Banja la Ana Opeza Lingachite Kuti Lizigwirizana ndi Anthu Ena

Kodi mfundo za m’Baibulo zingathandize bwanji makolo a m’banja la ana opeza kuti azigwirizana ndi anzawo, achibale komanso makolo enieni a anawo?