Pitani ku nkhani yake

Nyimbo 56​—Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi

Nyimbo 56​—Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi

Imbirani limodzi ndi ana pamene akuimba nyimbo yosonyeza kuti akufuna kumakonda kwambiri choonadi.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Inuyo Panokha Muzikonda Kwambiri Choonadi

Kodi ndi zinthu ziti zimene mungachite zomwe zingakuthandizeni kuti muzikonda kwambiri choonadi?

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.