Nyimbo 120—Khalani Omvera Kuti Mulandire Madalitso
Tikhoza kukhala bwenzi la Yehova poimba nyimbo. Tiyeni tiimbe nyimbo limodzi ndi Kalebe ndi Sofiya. Nyimboyi ikunena za madalitso omwe tingapeze chifukwa chomvera Yehova.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
MAVIDIYO
Phunzirani kwa Anzake a Yehova
Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!
ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA
Zoti Ana Achite
Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.