ZOTI MUCHITE
Zimene Mungachite Mukakhumudwa
Zoti muchitezi zikuthandizani kuti musapitirize kukhala okhumudwa.
Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
Kodi Ndingatani Kuti Ndisamangoganizira Zinthu Zolakwika?
Mukhoza kumaganizira zinthu zabwino mukamatsatira mfundo zomwe zili mu nkhaniyi.
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
N’chiyani Chingandithandize Ndikakhala Ndi Nkhawa?
Zinthu 5 zimene zingakuthandizeni kuti muzida nkhawa pa zinthu zoyenera m’malo mwa zinthu zimene zingakubweretserani mavuto.
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
Kodi Ndine Wopirira?
Aliyense amakumana ndi mavuto, choncho m’pofunika kuphunzira kukhala wopirira, ngakhale mavutowo atakhala aang’ono kapena aakulu.
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
Kodi Ndingatani Ngati Ndili ndi Matenda Ovutika Maganizo?
Mfundo zomwe zili m’nkhaniyi zingakuthandizeni kudziwa zimene mungachite kuti muchire.
MAVIDIYO AMAKATUNI
Zimene Mungachite Kuti Muyambirenso Kusangalala
Kodi mungatani ngati mukukhalabe okhumudwa kwa nthawi yaitali?
ZIMENE ACHINYAMATA AMAFUNSA
Kodi Ndingatani Kuti Ndisamasinthesinthe Mmene Ndimamvera?
Anthu ambiri amasinthasintha mmene akumvera, koma zimenezi zimasokoneza ana ambiri. Koma chosangalatsa n’choti utha kudziwa bwino zimene zikukuchitikira komanso n’zotheka kupirira vutoli.
ZOTI ACHINYAMATA ACHITE