Turkey
Khoti Loona za Ufulu wa Anthu ku Ulaya Lagamula kuti Dziko la Turkey Liyenera Kuvomereza Nyumba za Ufumu Monga “Malo Olambirira”
Ngakhale kuti zinthu zakhala zikuyenda bwino kwa a Mboni za Yehova pankhani zamalamulo, iwo akuvutikabe chifukwa malamulo a dziko la Turkey sakuwalola kumanga komanso kukhala ndi malo olambirira ovomerezeka.
Khoti Loona za Ufulu wa Anthu ku Ulaya Lagamula Mlandu Wina Mokomera Anthu 4 a Mboni ku Turkey
Zimene khoti lachita poweruza mlandu wachitatu mosakomera boma la Turkey zikusonyezeratu kuti mayiko onse amene ali m’Bungwe la Mayiko a ku Ulaya, akuyenera kutsatira mfundo zimene zili m’Pangano Lokhudza Ufulu wa Anthu ku Ulaya, zomwe zimasonyeza kuti munthu aliyense ali ndi ufulu wokana kulowa usilikali.
Dziko la Turkey Likukana Kutsatira Mfundo Zimene Mayiko a ku Ulaya Amayendera Zokhudza Ufulu wa Anthu
N’chifukwa chiyani boma likukana kulemekeza ufulu umene anthu ali nawo wokana kulowa usilikali, womwe ndi ufulu wofunika kwambiri wokhudza ufulu wachibadwidwe?
Bungwe la UN Lauza Boma la Turkey Kuti Lizilemekeza Zimene Anthu a M’dzikolo Amakhulupirira
Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chigamulo chimene bungwe la UN linapereka chopatsa anthu a ku Turkey ufulu wokana kulowa usilikali chifukwa cha zimene amakhulupirira.