Pitani ku nkhani yake

Turkey

 

2016-11-02

TURKEY

Khoti Loona za Ufulu wa Anthu ku Ulaya Lagamula kuti Dziko la Turkey Liyenera Kuvomereza Nyumba za Ufumu Monga “Malo Olambirira”

Ngakhale kuti zinthu zakhala zikuyenda bwino kwa a Mboni za Yehova pankhani zamalamulo, iwo akuvutikabe chifukwa malamulo a dziko la Turkey sakuwalola kumanga komanso kukhala ndi malo olambirira ovomerezeka.

2014-06-17

TURKEY

Khoti Loona za Ufulu wa Anthu ku Ulaya Lagamula Mlandu Wina Mokomera Anthu 4 a Mboni ku Turkey

Zimene khoti lachita poweruza mlandu wachitatu mosakomera boma la Turkey zikusonyezeratu kuti mayiko onse amene ali m’Bungwe la Mayiko a ku Ulaya, akuyenera kutsatira mfundo zimene zili m’Pangano Lokhudza Ufulu wa Anthu ku Ulaya, zomwe zimasonyeza kuti munthu aliyense ali ndi ufulu wokana kulowa usilikali.

2014-04-10

TURKEY

Dziko la Turkey Likukana Kutsatira Mfundo Zimene Mayiko a ku Ulaya Amayendera Zokhudza Ufulu wa Anthu

N’chifukwa chiyani boma likukana kulemekeza ufulu umene anthu ali nawo wokana kulowa usilikali, womwe ndi ufulu wofunika kwambiri wokhudza ufulu wachibadwidwe?

2013-12-31

TURKEY

Bungwe la UN Lauza Boma la Turkey Kuti Lizilemekeza Zimene Anthu a M’dzikolo Amakhulupirira

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe chigamulo chimene bungwe la UN linapereka chopatsa anthu a ku Turkey ufulu wokana kulowa usilikali chifukwa cha zimene amakhulupirira.