Pitani ku nkhani yake

Nkhani za Padziko Lonse

 

2024-03-15

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2024

Mu lipotili, tiona mmene Atate wathu wachikondi Yehova, amasonyezera kuti “akufuna kuti anthu onse alape.” (2 Pet. 3:9) Tionanso zinthu zina zimene zasintha pa nkhani ya mmene tiyenera kuvalira tikamachita zinthu zauzimu.

2024-01-29

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 1 la 2024

Onani mmene kukonda anthu kungatithandizire kuti tizichita khama mu utumiki.

2023-12-18

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2023

Onani mmene timasonyezera kuti ndife atumiki a Mulungu posankha zinthu mwanzeru pankhani ya zovala ndi kudzikongoletsa komanso mmene tingalimbikitsire mgwirizano mumpingo.

2023-08-25

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 6 la 2023

Mu lipotili, m’bale wa M’Bungwe Lolamulira akutionetsa vidiyo yolimbikitsa ya m’bale Negede Teklemariam.

2023-08-03

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 5 la 2023

Mu lipotili, m’bale wa m’Bungwe Lolamulira akutionetsa vidiyo yolimbikitsa ya m’bale Dennis Christensen ndi mkazi wake Irina.

2023-05-26

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2023

Mu lipotili m’bale wa m’Bungwe Lolamulira akutithandiza kuti tiyembekezere mwachidwi misonkhano ya chigawo ya pamasom’pamaso, akufotokozanso mmene Yehova amatitetezera mwauzimu

2023-04-17

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2023

M’bale wa m’Bungwe Lolamulira akufotokoza zimene abale athu akuchita posonyeza kuti akupanga Yehova kukhala malo awo othawirapo ngakhale kuti akukumana ndi mavuto.

2023-03-15

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2023

M’bale wa m’Bungwe Lolamulira akupereka lipoti lokhudza abale ndi alongo athu a ku Türkiye komanso akucheza ndi abale awiri.

2023-01-06

NKHANI ZA PADZIKO LONSE

Lipoti Loyamba la Bungwe Lolamulira la 2023

Tikukulimbikitsani kuti muonere lipotili kuti mumve zilengezo zosangalatsa kwambiri zokhudza ntchito yomanga ya ku Ramapo komanso zokhudza apainiya.