Nkhani za Padziko Lonse
Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2024
Mu lipotili, tiona mmene Atate wathu wachikondi Yehova, amasonyezera kuti “akufuna kuti anthu onse alape.” (2 Pet. 3:9) Tionanso zinthu zina zimene zasintha pa nkhani ya mmene tiyenera kuvalira tikamachita zinthu zauzimu.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 1 la 2024
Onani mmene kukonda anthu kungatithandizire kuti tizichita khama mu utumiki.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 8 la 2023
Onani mmene timasonyezera kuti ndife atumiki a Mulungu posankha zinthu mwanzeru pankhani ya zovala ndi kudzikongoletsa komanso mmene tingalimbikitsire mgwirizano mumpingo.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 6 la 2023
Mu lipotili, m’bale wa M’Bungwe Lolamulira akutionetsa vidiyo yolimbikitsa ya m’bale Negede Teklemariam.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 5 la 2023
Mu lipotili, m’bale wa m’Bungwe Lolamulira akutionetsa vidiyo yolimbikitsa ya m’bale Dennis Christensen ndi mkazi wake Irina.
Lipoti la Bungwe Lolamulira la Nambala 4 la 2023
Mu lipotili m’bale wa m’Bungwe Lolamulira akutithandiza kuti tiyembekezere mwachidwi misonkhano ya chigawo ya pamasom’pamaso, akufotokozanso mmene Yehova amatitetezera mwauzimu
Lipoti Lachitatu la Bungwe Lolamulira la 2023
M’bale wa m’Bungwe Lolamulira akufotokoza zimene abale athu akuchita posonyeza kuti akupanga Yehova kukhala malo awo othawirapo ngakhale kuti akukumana ndi mavuto.
Lipoti Lachiwiri la Bungwe Lolamulira la 2023
M’bale wa m’Bungwe Lolamulira akupereka lipoti lokhudza abale ndi alongo athu a ku Türkiye komanso akucheza ndi abale awiri.
Lipoti Loyamba la Bungwe Lolamulira la 2023
Tikukulimbikitsani kuti muonere lipotili kuti mumve zilengezo zosangalatsa kwambiri zokhudza ntchito yomanga ya ku Ramapo komanso zokhudza apainiya.