Pitani ku nkhani yake

Pitani ku mitu ya nkhani

Kodi Tingadziwe Bwanji Kuti Baibulo Limanena Zoona?

Kodi Tingadziwe Bwanji Kuti Baibulo Limanena Zoona?

Baibulo limanena kuti malemba onse ndi ochokera kwa Mulungu ndipo iye “sanganame.” (1 Atesalonika 2:13; Tito 1:2) Kodi zimenezi ndi zoona kapena Baibulo ndi buku la nthano chabe?